Mateyu 22:32 - Buku Lopatulika32 Ine ndili Mulungu wa Abrahamu, ndi Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo? Sali Mulungu wa akufa koma wa amoyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ine ndili Mulungu wa Abrahamu, ndi Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo? Sali Mulungu wa akufa koma wa amoyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 ‘Ine ndine Mulungu wa Abrahamu, ndine Mulungu wa Isaki, ndine Mulungu wa Yakobe?’ Ndiye kutitu sali Mulungu wa anthu akufa ai, koma wa anthu amoyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 ‘Ine ndine Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isake ndi Mulungu wa Yakobo?’ Iyeyo si Mulungu wa akufa koma wa amoyo.” Onani mutuwo |