Mateyu 22:31 - Buku Lopatulika31 Koma za kuuka kwa akufa, simunawerenge kodi chomwe chinanenedwa kwa inu ndi Mulungu, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma za kuuka kwa akufa, simunawerenga kodi chomwe chinanenedwa kwa inu ndi Mulungu, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Tsono zakuti anthu adzauka kwa akufa, kodi simudaŵerenge zimene Mulungu adakuuzani zija kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Koma za kuukitsidwa kwa akufa, kodi simunawerenge zimene Mulungu ananena kwa inu kuti, Onani mutuwo |