Mateyu 22:30 - Buku Lopatulika30 Pakuti m'kuuka kwa akufa sakwatira, kapena kukwatiwa, koma akhala ngati angelo a Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pakuti m'kuuka kwa akufa sakwatira, kapena kukwatiwa, koma akhala ngati angelo a Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Pajatu pouka akufa, palibenso za kukwatira kapena kukwatiwa ai. Onse ali ngati angelo Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Anthu akadzaukitsidwa, sadzakwatira kapena kukwatiwa; adzakhala ngati angelo kumwamba. Onani mutuwo |