Mateyu 22:29 - Buku Lopatulika29 Koma Yesu anayankha, nati kwa iwo, Mungolakwa osadziwa malembo, kapena mphamvu za Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Koma Yesu anayankha, nati kwa iwo, Mungolakwa osadziwa malembo, kapena mphamvu za Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adaŵayankha kuti, “Mukulakwa chifukwa simudziŵa Malembo, ngakhalenso mphamvu za Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Yesu anayankha kuti, “Inu mukulakwitsa chifukwa simukudziwa malemba kapena mphamvu ya Mulungu. Onani mutuwo |