Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 22:28 - Buku Lopatulika

28 Chifukwa chake m'kuuka kwa akufa, iye adzakhala mkazi wa yani wa asanu ndi awiriwo? Pakuti onse anakhala naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Chifukwa chake m'kuuka kwa akufa, iye adzakhala mkazi wa yani wa asanu ndi awiriwo? Pakuti onse anakhala naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Nanga tsono pa tsiku lodzauka akufa, mwini mkaziyo adzakhala utiwuti pakati pa abale asanu ndi aŵiri aja, popeza kuti onsewo adaamkwatirapo?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Tsopano, kodi akadzaukitsidwa adzakhala mkazi wa ndani mwa asanu ndi awiriwa popeza aliyense anamukwatirapo?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 22:28
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pomalizira anamwaliranso mkaziyo.


Koma Yesu anayankha, nati kwa iwo, Mungolakwa osadziwa malembo, kapena mphamvu za Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa