Mateyu 22:24 - Buku Lopatulika24 nanena, Mphunzitsi, Mose anati, Ngati munthu akafa wopanda mwana, mphwake adzakwatira mkazi wake, nadzamuukitsira mbale wake mbeu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 nanena, Mphunzitsi, Mose anati, Ngati munthu akafa wopanda mwana, mphwake adzakwatira mkazi wake, nadzamuukitsira mbale wake mbeu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 “Aphunzitsi, Mose adati, ‘Ngati munthu amwalira opanda ana, mbale wake wa womwalirayo aloŵe chokolo, kuti amuberekere ana mbale wake uja.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iwo anati, “Aphunzitsi, Mose anatiwuza kuti munthu akamwalira wosasiya ana, mʼbale wake akuyenera kukwatira mkazi wamasiyeyo kuti amuberekere ana mʼbale wakeyo. Onani mutuwo |