Mateyu 22:18 - Buku Lopatulika18 Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Yesu anadziwa kuipa kwao, nati, Mundiyeseranji Ine, onyenga inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma Yesu podziŵa maganizo ao oipa, adati, “Bwanji kodi mukundiyesa dala, anthu achiphamasonu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma Yesu podziwa maganizo awo oyipa anati, “Inu achiphamaso, bwanji mufuna kundipezera chifukwa? Onani mutuwo |