Mateyu 22:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa chake mutiuze ife, muganiza chiyani? Kuloledwa kodi kupatsa msonkho kwa Kaisara, kapena iai? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa chake mutiuze ife, muganiza chiyani? Kuloledwa kodi kupatsa msonkho kwa Kaisara, kapena iai? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndiye timati mutiwuze zimene mukuganiza. Kodi Malamulo a Mulungu amatilola kuti tizikhoma msonkho kwa Mfumu ya ku Roma, kapena ai?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tiwuzeni tsono maganizo anu ndi otani, kodi nʼkololedwa kupereka msonkho kwa Kaisara kapena ayi?” Onani mutuwo |