Mateyu 22:11 - Buku Lopatulika11 Koma mfumuyo m'mene inadza kuwaona akudyawo, anapenya momwemo munthu wosavala chovala cha ukwati; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma mfumuyo m'mene inadza kuwaona akudyawo, anapenya momwemo munthu wosavala chovala cha ukwati; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Pamene mfumu ija idaloŵa m'nyumbamo kukaona anthu odzadya phwando aja, idapezamo wina amene sadavale chovala chaukwati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Koma pamene mfumu inabwera kudzaona oyitanidwawo, inaona munthu amene sanavale zovala zaukwati. Onani mutuwo |