Mateyu 22:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo akapolo ao anatulukira kunjira, nasonkhanitsa onse amene anawapeza, ngakhale oipa, ngakhale abwino; ndipo ukwatiwo unadzala ndi okhala pachakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo akapolo ao anatulukira kunjira, nasonkhanitsa onse amene anawapeza, ngakhale oipa, ngakhale abwino; ndipo ukwatiwo unadzala ndi okhala pachakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Apo antchitowo adapitadi ku miseu nakasonkhanitsa onse amene adaŵapeza, abwino ndi oipa omwe, mwakuti nyumba yaphwando idadzaza ndi anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pamenepo antchitowo anapita ku misewu nakasonkhanitsa anthu onse amene anakawapeza, abwino ndi oyipa omwe, ndipo nyumba ya madyerero inadzaza ndi oyitanidwa. Onani mutuwo |