Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 21:7 - Buku Lopatulika

7 nabwera ndi bulu ndi mwana wake, naika pa iwo zovala zao, nakhala Iye pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 nabwera ndi bulu ndi mwana wake, naika pa iwo zovala zao, nakhala Iye pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Adabwera naye bulu ndi mwana wake uja, nayala zovala zao pamsana pa abuluwo, Yesu nkukwerapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Anabweretsa bulu ndi mwana wake, nayala zovala zawo pa abuluwo, ndipo Yesu anakwerapo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 21:7
6 Mawu Ofanana  

Nafulumira iwo, nagwira yense chofunda chake, nachiyala pokhala iye pachiunda, naomba lipenga, nati, Yehu ndiye mfumu.


nanena kwa iwo, Mukani kumudzi wopenyana ndi inu, ndipo pomwepo mudzapeza bulu womangidwa, ndi mwana wake pamodzi naye, masulani iwo, mudze nao kwa Ine.


Ndipo ophunzirawo anamuka, nachita monga Yesu anawauza;


Ndipo ambirimbiri a mpingowo anayala zovala zao panjira; ndipo ena anadula nthambi za mitengo, naziyala m'njiramo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa