Mateyu 21:7 - Buku Lopatulika7 nabwera ndi bulu ndi mwana wake, naika pa iwo zovala zao, nakhala Iye pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 nabwera ndi bulu ndi mwana wake, naika pa iwo zovala zao, nakhala Iye pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adabwera naye bulu ndi mwana wake uja, nayala zovala zao pamsana pa abuluwo, Yesu nkukwerapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anabweretsa bulu ndi mwana wake, nayala zovala zawo pa abuluwo, ndipo Yesu anakwerapo. Onani mutuwo |