Mateyu 21:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tsono adamugwiradi, namuponya kunja kwa mundawo, nkumupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Pamenepo anamutenga namuponyera kunja kwa munda wamphesa namupha. Onani mutuwo |