Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 21:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Tsono adamugwiradi, namuponya kunja kwa mundawo, nkumupha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Pamenepo anamutenga namuponyera kunja kwa munda wamphesa namupha.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 21:39
16 Mawu Ofanana  

Koma olimawo m'mene anaona mwanayo, ananena wina ndi mnzake, Uyo ndiye wolowa; tiyeni, timuphe, ndipo ife tidzatenga cholowa chake.


Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani?


Ndipo Yesu anati kwa iye, Mnzanga, wafikiranji iwe? Pomwepo iwo anadza, namthira Yesu manja, namgwira Iye.


Ndipo iwo akugwira Yesu ananka naye kwa Kayafa, mkulu wa ansembe, kumene adasonkhana alembi ndi akulu omwe.


Ndipo khamulo ndi kapitao wamkulu, ndi anyamata a Ayuda anagwira Yesu nammanga Iye,


Koma Anasi adamtumiza Iye womangidwa kwa Kayafa mkulu wa ansembe.


ameneyo, woperekedwa ndi uphungu woikidwa ndi kudziwiratu kwa Mulungu, inu mwampachika ndi kumupha ndi manja a anthu osaweruzika;


zindikirani inu nonse, ndi anthu onse a Israele, kuti m'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, amene inu munampachika pamtanda, amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa, mwa Iyeyu munthuyu aimirirapo pamaso panu, wamoyo.


Mulungu wa makolo athu anaukitsa Yesu, amene munamupha inu, ndi kumpachika pamtengo.


Ndiye yani wa aneneri makolo anu sanamzunze? Ndipo anawapha iwo amene anaonetseratu za kudza kwake kwa Wolungamayo; wa Iye amene mwakhala tsopano akumpereka ndi akumupha;


Munamtsutsa, munapha wolungamayo, iye sakaniza inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa