Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 21:40 - Buku Lopatulika

40 Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 “Kodi mwini munda wamphesa uja akadzafika, adzaŵatani alimi aja?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 “Tsono akabwera mwini munda wamphesa adzachita nawo chiyani matenantiwo?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 21:40
7 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano, inu okhala mu Yerusalemu, ndi anthu a Yuda, weruzanitu mlandu wa ine ndi munda wanga wampesa.


Ndipo pamene nyengo ya zipatso inayandikira, anatumiza akapolo ake kwa olima mundawo, kukalandira zipatso zake.


Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.


Iwo ananena kwa Iye, Adzaononga koipa oipawo, nadzapereka mundawo kwa olima ena, amene adzambwezera iye zipatso pa nyengo zake.


Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena.


ndipo mutani, kulanga koposa kotani nanga adzayesedwa woyenera iye amene anapondereza Mwana wa Mulungu, nayesa mwazi wa chipangano umene anayeretsedwa nao chinthu wamba, nachitira chipongwe Mzimu wa chisomo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa