Mateyu 21:40 - Buku Lopatulika40 Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 “Kodi mwini munda wamphesa uja akadzafika, adzaŵatani alimi aja?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 “Tsono akabwera mwini munda wamphesa adzachita nawo chiyani matenantiwo?” Onani mutuwo |