Mateyu 21:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo pamene nyengo ya zipatso inayandikira, anatumiza akapolo ake kwa olima mundawo, kukalandira zipatso zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo pamene nyengo ya zipatso inayandikira, anatumiza akapolo ake kwa olima mundawo, kukalandira zipatso zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Nyengo yothyola zipatso itayandikira, munthu uja adatuma antchito ake kwa alimi aja, kuti akatengeko zipatso za m'munda muja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Pamene nthawi yokolola inakwana, anatumiza antchito ake kwa matenanti aja kuti akatenge zipatso zake. Onani mutuwo |