Mateyu 21:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo olimawo anatenga akapolo ake, nampanda mmodzi, wina namupha, wina namponya miyala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo olimawo anatenga akapolo ake, nampanda mmodzi, wina namupha, wina namponya miyala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Koma alimiwo adaŵagwira antchito aja, wina kummenya, wina kumupha, wina kumponya miyala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 “Alimi aja anagwira antchito ake; namenya mmodzi, napha wina, ndi kumuponya miyala wachitatuyo. Onani mutuwo |