Mateyu 21:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo munthu akanena kanthu ndi inu, mudzati, Ambuye asowa iwo, ndipo pomwepo adzawatumiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo munthu akanena kanthu ndi inu, mudzati, Ambuye asowa iwo, ndipo pomwepo adzawatumiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Wina akakakufunsani kanthu, inu mukati, ‘Ambuye ali nawo ntchito, akangothana nawo aŵatumiza nthaŵi yomweyo.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Wina akakayankhula, mukamuwuze kuti Ambuye akuwafuna, ndipo adzawatumiza nthawi yomweyo.” Onani mutuwo |