Mateyu 21:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo ophunzira poona ichi anazizwa, nati, Mkuyuwo unafota bwanji msanga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo ophunzira poona ichi anazizwa, nati, Mkuyuwo unafota bwanji msanga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pamene ophunzira aja adaona zimenezi, adadabwa nafunsa Yesu kuti, “Mkuyuwu wauma bwanji nthaŵi yomweyi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ophunzira ataona zimenezi, anadabwa nafunsa kuti, “Kodi mtengo wamkuyuwu wauma msanga bwanji?” Onani mutuwo |