Mateyu 21:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo makamu a anthu anati, Uyu ndi mneneri Yesu wa ku Nazarete wa ku Galileya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo makamu a anthu anati, Uyu ndi mneneri Yesu wa ku Nazarete wa ku Galileya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono onse aja adayankha kuti, “Ameneyu ndi mneneri Yesu wochokera ku Nazarete, ku Galileya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Magulu a anthu anayankha kuti, “Uyu ndi Yesu, mneneri wochokera ku Nazareti.” Onani mutuwo |