Mateyu 21:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo m'mene adalowa mu Yerusalemu mzinda wonse unasokonezeka, nanena, Ndani uyu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo m'mene adalowa m'Yerusalemu mudzi wonse unasokonezeka, nanena, Ndani uyu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pamene Yesu adaloŵa mu Yerusalemu, mzinda wonse udatekeseka, ena nkumafunsa kuti, “Kodi ameneyu ndani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Yesu atalowa mu Yerusalemu, mzinda wonse unatekeseka ndipo anthu anafunsa kuti, “Ndani ameneyu?” Onani mutuwo |