Mateyu 20:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Yesu adaima, naŵaitana, nkuŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna kuti ndikuchitireni chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Yesu anayima ndi kuwayitana ndipo anawafunsa kuti, “Mukufuna ndikuchitireni chiyani?” Onani mutuwo |