Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 20:33 - Buku Lopatulika

33 Ananena kwa Iye, Ambuye, kuti maso athu apenye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ananena kwa Iye, Ambuye, kuti maso athu apenye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Iwo aja adati, “Ambuye, tikufuna kuti tizipenya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Anamuyankha nati, “Ambuye, tikufuna tione!”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 20:33
4 Mawu Ofanana  

Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu.


Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani?


Ndipo Yesu anagwidwa ndi chifundo, nakhudza maso ao; ndipo pomwepo anapenyanso, namtsata Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa