Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 20:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo khamulo linawaletsa, kuti atonthole: koma anakuwitsa, nanena, Ambuye, mutichitire chifundo, Inu Mwana wa Davide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo khamulo linawaletsa, kuti atonthole: koma anakuwitsa, nanena, Ambuye, mutichitire chifundo, Inu Mwana wa Davide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Anthu aja adaŵazazira akhunguwo kuti akhale chete. Koma iwo nkumafuulirafuulira kuti, “Inu Ambuye, Mwana wa Davide, mutichitire chifundo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Gulu la anthulo linawadzudzula iwo ndi kuwawuza kuti akhale chete, koma anafuwulitsabe kuti, “Ambuye, Mwana wa Davide, tichitireni chifundo!”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 20:31
12 Mawu Ofanana  

Koma Iye sanamyankhe mau amodzi. Ndipo ophunzira ake anadza, nampempha, nati, Mumuuze amuke; pakuti afuula pambuyo pathu.


Pamenepo anadza nato tiana kwa Iye, kuti Iye aike manja ake pa ito, ndi kupemphera: koma ophunzirawo anawadzudzula.


Ndipo onani, anthu akhungu awiri anakhala m'mphepete mwa njira; m'mene iwo anamva kuti Yesu analikupitirirapo, anafuula nati, Mutichitire ife chifundo, Inu Mwana wa Davide.


Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani?


Ndipo popita Yesu kuchokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, ofuula ndi kuti, Mutichitire ife chifundo, mwana wa Davide.


Ndipo iwo akutsogolera anamdzudzula iye, kuti akhale chete; koma iye anafuulitsa chifuulire, Mwana wa Davide, mundichitire chifundo.


Chitani khama m'kupemphera, nimudikire momwemo ndi chiyamiko;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa