Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 20:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo pamene iwo analikutuluka mu Yeriko, khamu lalikulu la anthu linamtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo pamene iwo analikutuluka m'Yeriko, khamu lalikulu la anthu linamtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Pamene Yesu ndi ophunzira ake ankatuluka mu mzinda wa Yeriko, anthu ambirimbiri ankamutsatira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Pamene Yesu ndi ophunzira ake ankachoka ku Yeriko, gulu lalikulu la anthu linawatsata.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 20:29
3 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa