Mateyu 20:28 - Buku Lopatulika28 monga Mwana wa Munthu sanadze kutumikiridwa koma kutumikira, ndi kupereka moyo wake dipo la anthu ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 monga Mwana wa Munthu sanadze kutumikiridwa koma kutumikira, ndi kupereka moyo wake dipo la anthu ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Chitani monga m'mene adachitira Mwana wa Munthu: adabwera osati kuti ena adzamtumikire ai, koma kuti Iyeyo adzatumikire anthu ndi kupereka moyo wake kuti aombole anthu ochuluka.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Momwenso Mwana wa Munthu sanabwere kudzatumikiridwa, koma kudzatumikira, ndi kupereka moyo wake kukhala dipo la anthu ambiri.” Onani mutuwo |