Mateyu 20:15 - Buku Lopatulika15 Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Sikuloleka kwa ine kodi kuchita chimene ndifuna ndi zanga? Kapena diso lako laipa kodi chifukwa ine ndili wabwino? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kodi zinthu zanga ndisachite nazo monga ndifunira? Kapenatu ukuipidwa nawo ufulu wanga eti?’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kodi ndilibe ufulu wochita zimene ndikufuna ndi ndalama zanga? Kapena ukuyipidwa chifukwa ndine wopereka mowolowamanja?’ Onani mutuwo |