Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 2:17 - Buku Lopatulika

17 Pomwepo chinachitidwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Pomwepo chinachitidwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pamenepo zidachitikadi zimene mneneri Yeremiya adaanena kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Pamenepo, zimene ananena mneneri Yeremiya zinakwaniritsidwa:

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 2:17
5 Mawu Ofanana  

Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini;


nakhalabe kumeneko kufikira atamwalira Herode; kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Ambuye mwa mneneri kuti, Ndinaitana Mwana wanga atuluke mu Ejipito.


Pamenepo Herode, poona kuti anampusitsa Anzeruwo, anapsa mtima ndithu, natumiza ena kukaononga tiana tonse ta mu Betelehemu ndi ta m'midzi yake yonse, takufikira zaka ziwiri ndi tating'ono tonse, monga mwa nthawi imeneyo iye anafunsitsa kwa Anzeruwo.


Mau anamveka mu Rama, maliro ndi kuchema kwambiri; Rakele wolira ana ake, wosafuna kusangalatsidwa, chifukwa palibe iwo.


Pamenepo chinakwaniridwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, ndi kuti, Ndipo iwo anatenga ndalamazo zasiliva makumi atatu, mtengo wa uja wowerengedwa mtengo wake, amene iwo a ana a Israele anawerenga mtengo wake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa