Mateyu 2:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo iye ananyamuka natenga kamwana ndi amake usiku, nachoka kupita ku Ejipito; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo iye ananyamuka natenga kamwana ndi amake usiku, nachoka kupita ku Ejipito; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Apo Yosefe adadzuka usiku womwewo, nkutenga mwanayo ndi mai wake kupita ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Atadzuka, Yosefe anatenga mwanayo ndi amayi ake usiku omwewo napita ku Igupto, Onani mutuwo |