Mateyu 19:27 - Buku Lopatulika27 Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pamenepo Petro adayankhapo kuti, “Ifetu paja tidasiya zonse kuti tizikutsatani. Tsono ndiye kuti tidzalandira chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Petro anamuyankha Iye kuti, “Ife tinasiya zonse ndi kukutsatirani Inu! Nanga tsono ife tidzalandira chiyani?” Onani mutuwo |