Mateyu 19:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Yesu anawayang'ana, nati kwa iwo, Ichi sichitheka ndi anthu, koma zinthu zonse zitheka ndi Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Yesu anawayang'ana, nati kwa iwo, Ichi sichitheka ndi anthu, koma zinthu zonse zitheka ndi Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Yesu adaŵayang'ana nati, “Kwa anthu zimenezi nzosatheka, koma zonse nzotheka ndi Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Yesu anawayangʼana iwo nati, “Ndi anthu, izi nʼzosatheka, koma ndi Mulungu zinthu zonse zimatheka.” Onani mutuwo |