Mateyu 19:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo ophunzira, pamene anamva, anazizwa kwambiri, nanena, Ngati nkutero angapulumuke ndani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo ophunzira, pamene anamva, anazizwa kwambiri, nanena, Ngati nkutero angapulumuke ndani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Pamene ophunzira aja adamva zimenezi, adadabwa kwambiri nati, “Tsono nanga angathe kupulumuka ndani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ophunzira atamva zimenezi, anadabwa kwambiri ndipo anamufunsa kuti, “Nanga angapulumuke ndani?” Onani mutuwo |