Mateyu 19:14 - Buku Lopatulika14 Koma Yesu anati, Tilekeni tiana, musatikanize kudza kwa Ine: chifukwa Ufumu wa Kumwamba uli wa totere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma Yesu anati, Tilekeni tiana, musatikanize kudza kwa Ine: chifukwa Ufumu wa Kumwamba uli wa totere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma Yesu adati, “Alekeni anaŵa azibwera kwa Ine, musaŵaletse. Paja Ufumu wakumwamba ndi wa anthu otere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yesu anati, “Lolani ana abwere kwa Ine, ndipo musawaletse pakuti ufumu wakumwamba ndi wa iwo onga anawa.” Onani mutuwo |