Mateyu 19:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Iye anaika manja ake pa ito, nachokapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Iye anaika manja ake pa ito, nachokapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Atatero adaŵasanjika manja, kenaka nkumapita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Atasanjika manja ake pa anawo, anachokapo. Onani mutuwo |