Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 19:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo Iye anaika manja ake pa ito, nachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo Iye anaika manja ake pa ito, nachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Atatero adaŵasanjika manja, kenaka nkumapita.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Atasanjika manja ake pa anawo, anachokapo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 19:15
6 Mawu Ofanana  

Iye adzadyetsa zoweta zake ngati mbusa, nadzasonkhanitsa anaankhosa m'manja mwake, nadzawatengera pa chifuwa chake, ndipo adzatsogolera bwinobwino zimene ziyamwitsa.


Koma Yesu anati, Tilekeni tiana, musatikanize kudza kwa Ine: chifukwa Ufumu wa Kumwamba uli wa totere.


Ndipo onani, munthu anadza kwa Iye, nati, Mphunzitsi, chabwino nchiti ndichichite, kuti ndikhale nao moyo wosatha?


Ndipo Iye anatiyangata, natidalitsa, ndi kuika manja ake pa ito.


Pakuti mwamuna wosakhulupirirayo ayeretsedwa mwa mkaziyo, ndi mkazi wosakhulupirira ayeretsedwa mwa mbaleyo; ngati sikukadatero, ana anu akadakhala osakonzeka, koma tsopano akhala oyera.


ndi kuti kuyambira ukhanda wako wadziwa malembo opatulika, okhoza kukupatsa nzeru kufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa