Mateyu 19:11 - Buku Lopatulika11 Koma Iye anati kwa iwo, Onse sangathe kulandira chonena ichi, koma kwa iwo omwe chapatsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma Iye anati kwa iwo, Onse sangathe kulandira chonena ichi, koma kwa iwo omwe chapatsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Yesu adaŵauza kuti, “Si anthu onse angamvetse zimenezi ai, koma okhawo amene Mulungu aŵathandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yesu anayankha kuti, “Si aliyense amene angavomere chiphunzitso ichi, koma kwa okhawo amene achimvetsetsa. Onani mutuwo |