Mateyu 19:10 - Buku Lopatulika10 Ophunzira ananena kwa Iye, Ngati mlandu wa munthu ndi mkazi wake uli wotere, sikuli kwabwino kukwatira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ophunzira ananena kwa Iye, Ngati mlandu wa munthu ndi mkazi wake uli wotere, sikuli kwabwino kukwatira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ophunzira ake adamuuza kuti, “Ndiyetu ngati zili choncho pakati pa mwamuna ndi mkazi wake, ndi bwino tsono kusakwatira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ophunzira ake anati kwa Iye, “Ngati umu ndi mmene zilili pa mwamuna ndi mkazi, kuli bwino kusakwatira.” Onani mutuwo |