Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 18:1 - Buku Lopatulika

1 Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Nthawi yomweyo ophunzira anadza kwa Yesu, nanena, Ndani kodi ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Nthaŵi yomweyo ophunzira aja adadzamufunsa Yesu kuti, “Kodi mu Ufumu wakumwamba wamkulu koposa onse ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Pa nthawi imeneyo ophunzira anabwera kwa Yesu ndipo anamufunsa kuti, “Wamkulu woposa onse ndani mu ufumu wakumwamba?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 18:1
13 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Yesu anaitana kamwana, anakaimitsa pakati pao,


Koma wamkulu wopambana wa inu adzakhala mtumiki wanu.


nanena, Tembenukani mitima; chifukwa Ufumu wa Kumwamba wayandikira.


Si yense wakunena kwa Ine, Ambuye, Ambuye, adzalowa mu Ufumu wa Kumwamba; koma wakuchitayo chifuniro cha Atate wanga wa Kumwamba.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


musachite kanthu monga mwa chotetana, kapena monga mwa ulemerero wopanda pake, komatu ndi kudzichepetsa mtima, yense ayese anzake omposa iye mwini;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa