Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 17:15 - Buku Lopatulika

15 Ambuye, chitirani mwana wanga chifundo; chifukwa adwala khunyu, kuzunzika koipa: pakuti amagwa kawirikawiri pamoto, ndi kawirikawiri m'madzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ambuye, chitirani mwana wanga chifundo; chifukwa adwala nkhunyu, kuzunzika koipa: pakuti amagwa kawirikawiri pamoto, ndi kawirikawiri m'madzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Adati, “Ambuye mchitireni chifundo mwana wanga. Ali ndi khunyu ndipo amavutika koopsa. Kaŵirikaŵiri amagwa pa moto mwinanso m'madzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Iye anati, “Ambuye, muchitireni chifundo mwana wanga akudwala matenda akugwa ndipo akuvutika kwambiri. Kawirikawiri iye amagwa pa moto kapena mʼmadzi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 17:15
14 Mawu Ofanana  

Natuluka Satana pamaso pa Yehova, nazunza Yobu ndi zilonda zowawa, kuyambira kuphazi lake kufikira pakati pamutu pake.


Ndipo onani, mkazi wa ku Kanani anatuluka m'malire, nafuula, nati, Mundichitire ine chifundo Ambuye, mwana wa Davide; mwana wanga wamkazi wagwidwa koopsa ndi chiwanda.


Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa.


Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


ndipo ovutidwa ndi mizimu yonyansa anachiritsidwa,


Koma Yudasinso amene akampereka Iye, anadziwa malowa; chifukwa Yesu akankako kawirikawiri ndi ophunzira ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa