Mateyu 17:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndinabwera naye kwa ophunzira anuŵa, koma alephera kumchiritsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ine ndinabwera naye kwa ophunzira anu koma alephera kumuchiritsa.” Onani mutuwo |