Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 17:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ndinabwera naye kwa ophunzira anuŵa, koma alephera kumchiritsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ine ndinabwera naye kwa ophunzira anu koma alephera kumuchiritsa.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 17:16
7 Mawu Ofanana  

Ambuye, chitirani mwana wanga chifundo; chifukwa adwala khunyu, kuzunzika koipa: pakuti amagwa kawirikawiri pamoto, ndi kawirikawiri m'madzi.


Ndipo Yesu anayankha nati, Ha, obadwa osakhulupirira ndi amphulupulu, ndidzakhala ndi inu nthawi yanji? Ndidzalekerera inu nthawi yanji? Mudze naye kwa Ine kuno.


Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe.


Ndipo pa chikhulupiriro cha m'dzina lake dzina lakelo linalimbikitsa iye amene mumuona, nimumdziwa; ndipo chikhulupiriro chili mwa Iye chinampatsa kuchira konse kumeneku pamaso pa inu nonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa