Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 17:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo pamene iwo anadza kukhamu la anthu, kunafika kwa Iye munthu, namgwadira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo pamene iwo anadza kukhamu la anthu, kunafika kwa Iye munthu, namgwadira Iye, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pamene iwo adafikanso kumene kunali khamu la anthu kuja, munthu wina adadzagwadira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Atafika ku gulu la anthu, munthu wina anamuyandikira Yesu ndi kugwada pamaso pake.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 17:14
8 Mawu Ofanana  

Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.


Ndipo anadza kwa Iye wodwala khate, nampempha Iye, namgwadira, ndi kunena ndi Iye, Ngati mufuna mukhoza kundikonza.


Ndipo pamene Iye anatuluka kutsata njira, anamthamangira munthu, namgwadira Iye, namfunsa, Mphunzitsi wabwino, ndidzachita chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?


Ndipo kunali pamene tidatsiriza masikuwa, tidachoka ndi kunka ulendo wathu; ndipo iwo onse, akazi ndi ana, anatiperekeza kufikira kutuluka m'mzinda; ndipo pogwadira pa mchenga wa kunyanja, tinapemphera,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa