Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 17:13 - Buku Lopatulika

13 Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pamenepo ophunzira aja adazindikira kuti ankaŵauza za Yohane Mbatizi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pamenepo ophunzira anazindikira kuti amawawuza za Yohane Mʼbatizi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 17:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.


koma ndinena kwa inu, kuti Eliya anadza kale, ndipo iwo sanamdziwe iye, koma anamchitira zonse zimene anazifuna iwo. Ndipo chonchonso Mwana wa Munthu adzazunzidwa ndi iwo.


Ndipo pamene iwo anadza kukhamu la anthu, kunafika kwa Iye munthu, namgwadira Iye, nati,


Ndipo masiku aja anadza Yohane Mbatizi, nalalikira m'chipululu cha Yudeya,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa