Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 16:9 - Buku Lopatulika

9 Kodi chikhalire simudziwa, ndipo simukumbukira mikate isanu ija ya anthu aja zikwi zisanu, ndi madengu angati munawatola?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Kodi chikhalire simudziwa, ndipo simukumbukira mikate isanu ija ya anthu aja zikwi zisanu, ndi madengu angati munawatola?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kodi mpaka pano simunamvetsebe? Kodi simukukumbukira kuti ndi buledi msanu ndidadyetsa anthu zikwi zisanu? Nanga mudaadzaza madengu angati ndi zotsala?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kodi inu simukumvetsetsabe? Kodi simukukumbukira za buledi musanu amene anadya anthu 5,000 ndi madengu amene munadzaza?

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 16:9
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena nao, Mutero inunso opanda nzeru kodi? Kodi simuzindikira kuti kanthu kalikonse kochokera kunja kukalowa mwa munthu, sikangathe kumdetsa iye;


Simukumbukira kodi, kuti pokhala nanu, ndisanachoke ine, ndinakuuzani izi?


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa