Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 16:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo iwo anafunsana wina ndi mnzake, nati, Sitinatenge mikate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo iwo anafunsana wina ndi mnzake, nati, Sitinatenga mikate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Apo ophunzirawo adayamba kukambirana nkumati, “Akuterotu chifukwa sitidatenge buledi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Iwo anakambirana pakati pawo za izi ndipo anati, “Ichi nʼchifukwa chakuti sitinatenge buledi aliyense.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 16:7
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anati kwa iwo, Yang'anirani mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi ndi Asaduki.


Koma Yesu, m'mene anadziwa, anati, Ha, inu okhulupirira pang'ono, mufunsana chifukwa ninji wina ndi mnzake, kuti simunatenga mikate?


Ubatizo wa Yohane, uchokera kuti? Kumwamba kodi kapena kwa anthu? Koma iwo anafunsana wina ndi mnzake, kuti, Tikati, Kumwamba, Iye adzati kwa ife, Munalekeranji kumvera iye?


Ndipo anasunga mauwo, nafunsana mwa iwo okha, kuti, Kuuka kwa akufa nchiyani?


Ndipo kunali m'kukambirana kwao ndi kufunsana, Yesu mwini anayandikira, natsagana nao.


Ndipo anayamba kutsutsana kuti wamkulu mwa iwo ndani.


Koma Petro anati, Iaitu, Mbuye; pakuti sindinadye ine ndi kale lonse kanthu wamba ndi konyansa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa