Mateyu 16:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Afarisi ndi Asaduki anadza, namuyesa, namfunsa Iye awaonetse chizindikiro cha Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Afarisi ndi Asaduki anadza, namuyesa, namfunsa Iye awaonetse chizindikiro cha Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku lina kudabwera Afarisi ndi Asaduki ena kwa Yesu. Adampempha kuti aŵaonetse chizindikiro chozizwitsa chochokera kumwamba. Pakutero ankangofuna kumutchera msampha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Afarisi ndi Asaduki anabwera kwa Yesu ndi kumuyesa pomufunsa kuti awaonetse chizindikiro chochokera kumwamba. Onani mutuwo |