Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo m'mene Iye anauza makamuwo amuke, analowa m'ngalawa, nafika m'malire a Magadani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo m'mene Iye anauza makamuwo amuke, analowa m'ngalawa, nafika m'malire a Magadani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Pambuyo pake Yesu adatsazikana nawo anthu aja, kenaka Iye adaloŵa m'chombo napita ku dera la Magadani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Yesu atatha kuwuza gululo kuti lipite kwawo, analowa mʼbwato ndipo anapita kudera la Magadala.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:39
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pomwepo Iye anafulumiza ophunzira alowe m'ngalawa, ndi kumtsogolera Iye kutsidya lija, kufikira Iye atauza makamu amuke.


Ndipo anadyawo anali amuna zikwi zinai kuwaleka akazi ndi ana.


Ndipo anati kwa ophunzira ake, kuti kangalawa kamlinde Iye, chifukwa cha khamulo, kuti angamkanikize Iye,


Ndipo pomwepo analowa m'ngalawa ndi ophunzira ake, nafika ku mbali ya ku Dalamanuta.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa