Mateyu 15:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo anadyawo anali amuna zikwi zinai kuwaleka akazi ndi ana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo anadyawo anali amuna zikwi zinai kuwaleka akazi ndi ana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Koma tsono anthu amene adaadyawo, analipo zikwi zinai amuna okha, osaŵerenga akazi ndi ana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Chiwerengero cha anthu amene anadya chinali 4,000 kupatula amayi ndi ana. Onani mutuwo |