Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:25 - Buku Lopatulika

25 Koma iye anadza, namgwadira Iye, nanena, Ambuye, ndithangateni ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Koma iye anadza, namgwadira Iye, nanena, Ambuye, ndithangateni ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Mai uja adadzamgwadira nati, “Ambuye, ndithu thandizeni.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Mayiyo anabwera ndi kugwada pamaso pake, nati, “Ambuye ndithandizeni!”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:25
10 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati Ndileke ndimuke, chifukwa kulinkucha. Ndipo Yakobo anati, Sindidzakuleka iwe kuti umuke, ukapanda kundidalitsa ine.


inde, analimbana ndi wamthenga nampambana; analira, nampembedza Iye; anampeza Iye ku Betele, ndi kumeneko Iye analankhula ndi ife;


Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu.


Ndipo Iye anayankha, nati, Sichabwino kutenga mkate wa ana, ndi kuuponyera tiagalu.


Ndipo khamulo linawaletsa, kuti atonthole: koma anakuwitsa, nanena, Ambuye, mutichitire chifundo, Inu Mwana wa Davide.


Ndipo onani, wakhate anadza namgwadira Iye, nanena, Ambuye ngati mufuna mungathe kundikonza.


Ndipo kawirikawiri ukamtaya kumoto ndi kumadzi, kumuononga; koma ngati mukhoza kuchita kanthu mtithandize, ndi kutichitira chifundo.


Pomwepo atate wa mwana anafuula, nanena, Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa