Mateyu 15:25 - Buku Lopatulika25 Koma iye anadza, namgwadira Iye, nanena, Ambuye, ndithangateni ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma iye anadza, namgwadira Iye, nanena, Ambuye, ndithangateni ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Mai uja adadzamgwadira nati, “Ambuye, ndithu thandizeni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Mayiyo anabwera ndi kugwada pamaso pake, nati, “Ambuye ndithandizeni!” Onani mutuwo |