Mateyu 15:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Iye anayankha, nati, Sichabwino kutenga mkate wa ana, ndi kuuponyera tiagalu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Iye anayankha, nati, Sichabwino kutenga mkate wa ana, ndi kuuponyera tiagalu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Yesu adamuuza kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana nkuponyera agalu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Iye anayankha kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana ndi kuponyera agalu.” Onani mutuwo |