Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo Iye anayankha, nati, Sichabwino kutenga mkate wa ana, ndi kuuponyera tiagalu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo Iye anayankha, nati, Sichabwino kutenga mkate wa ana, ndi kuuponyera tiagalu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Yesu adamuuza kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana nkuponyera agalu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Iye anayankha kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana ndi kuponyera agalu.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:26
10 Mawu Ofanana  

Koma iye anadza, namgwadira Iye, nanena, Ambuye, ndithangateni ine.


Koma iye anati, Eetu, Ambuye, pakutinso tiagalu timadya nyenyeswa zakugwa pagome pa ambuye ao.


Musamapatsa chopatulikacho kwa agalu, ndipo musamaponya ngale zanu patsogolo pa nkhumba, kuti zingazipondereze ndi mapazi ao, ndi potembenuka zingang'ambe inu.


ndiwo Aisraele; ali nao umwana, ndi ulemerero, ndi mapangano, ndi kupatsa kwa malamulo, ndi kutumikira mu Kachisi wa Mulungu, ndi malonjezo;


Ife ndife Ayuda pachibadwidwe, ndipo sitili ochimwa a kwa amitundu;


kuti nthawi ija munali opanda Khristu, alendo a padera ndi mbumba ya Israele, ndi alendo alibe kanthu ndi mapangano a malonjezano, opanda chiyembekezo, ndi opanda Mulungu m'dziko lapansi.


Penyererani agalu, penyererani ochita zoipa, penyererani choduladula;


Kunja kuli agalu ndi anyanga, ndi achigololo, ndi ambanda, ndi opembedza mafano, ndi yense wakukonda bodza ndi kulichita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa