Mateyu 15:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo Iye anayankha, nati, Sindinatumidwa kwa ena koma kwa nkhosa zotayika za banja la Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo Iye anayankha, nati, Sindinatumidwa kwa ena koma kwa nkhosa zotayika za banja la Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Yesu adati, “Inetu Mulungu adandituma kwa amene ali ngati nkhosa zotayika pa mtundu wa Aisraele.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iye anayankha kuti, “Ine ndinatumidwa kwa nkhosa zotayika za Israeli zokha.” Onani mutuwo |