Mateyu 15:19 - Buku Lopatulika19 Pakuti mumtima muchokera maganizo oipa, zakupha, zachigololo, zachiwerewere, zakuba, za umboni wonama, zamwano; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pakuti mumtima muchokera maganizo oipa, zakupha, zachigololo, zachiwerewere, zakuba, za umboni wonama, zamwano; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Chifukwa m'kati mwa mitima ya anthu ndiye mumatuluka maganizo oipa, za kuphana, za chigololo, za chiwerewere, za kuba, maumboni onama, ndiponso zachipongwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pakuti mu mtima mumatuluka maganizo oyipa, zakupha, zachigololo, zadama, zakuba, zaumboni wonama ndi zachipongwe. Onani mutuwo |