Mateyu 15:20 - Buku Lopatulika20 izi ndizo ziipitsa munthu, koma kudya osasamba manja sikuipitsa munthu ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 izi ndizo ziipitsa munthu, koma kudya osasamba manja sikuipitsa munthu ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Zimenezi ndizo zimaipitsa munthu. Koma kudya chakudya osasamba m'manja, sikungaipitse munthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Izi ndi zimene zimachititsa munthu kukhala woyipa; koma kudya ndi mʼmanja mosasamba sikumuchititsa munthu kukhala woyipa.” Onani mutuwo |