Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:18 - Buku Lopatulika

18 Koma zakutuluka m'kamwa zichokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Koma zakutuluka m'kamwa zichokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Koma zotuluka m'kamwa mwa munthu zimachokera mu mtima, ndipo zimenezi ndizo zimamuipitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Koma zinthu zimene zituluka mʼkamwa zimachokera mu mtima ndipo zimenezi zimamuchititsa munthu kukhala woyipa.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:18
14 Mawu Ofanana  

Mau a pakamwa pake ndiwo opanda pake ndi onyenga, waleka kuzindikira ndi kuchita bwino.


Milomo ya wolungama idziwa zokondweretsa; koma m'kamwa mwa oipa munena zokhota.


Lilime la anzeru linena bwino zomwe adziwa; koma m'kamwa mwa opusa mutsanulira utsiru.


Mtima wa wolungama uganizira za mayankhidwe; koma m'kamwa mwa ochimwa mutsanulira zoipa.


Chinjiriza mtima wako koposa zonse uzisunga; pakuti magwero a moyo atulukamo.


Munthu wopanda pake, mwamuna wamphulupulu; amayenda ndi m'kamwa mokhota.


Akubadwa inu a njoka, mungathe bwanji kulankhula zabwino, inu akukhala oipa? Pakuti m'kamwa mungolankhula mwa kusefuka kwake kwa mtima.


si chimene chilowa m'kamwa mwake chiipitsa munthu; koma chimene chituluka m'kamwa mwake, ndicho chiipitsa munthu.


Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo?


Ndipo anati, Chotuluka mwa munthu ndicho chidetsa munthu.


Ananena kwa iye, Pakamwa pako ndikuweruza, kapolo woipa iwe. Unadziwa kuti ine ndine munthu wouma mtima, wonyamula chimene sindinachiike, ndi wotuta chimene sindinachifese;


Monga umanena mwambi wa makolo, kuti, Uchimo utulukira mwa ochimwa; koma dzanja langa silidzakhala pa inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa